Mkhalakale pa uwulutsi pa wayilesi, Lucius Chikuni, wamwalira

Katswiri komanso mkhalakale pa uwulutsi wa pa wayilesi, a Lucius Chikuni, amwalira pa chipatala cha Mwaiwathu munzinda wa Blantyre.


Chikuni yemwe amadziwika bwino chifukwa cha mawu ake okhathamira, wamwalira m’bandakucha wa lero Lolemba pa 10 February, 2025.


Kupatula kugwira ntchito ku wailesi za Malawi Broadcasting Corporation (MBC) komanso Zodiak, Chikuni ndi yemwenso adalemba sewero la John Chilembwe (Adaferanji).


Malemu Chikuni omwe adali ochokera ku dera la mfumu yaikulu Chimaliro m’boma la Thyolo, amwalira ali ndi zaka 84.


Related Articles

Dumped after victory: Sukez shares cautionary tale about politicians-

Dumped after victory: Sukez shares cautionary tale about politicians

Malawian filmmaker Sukez has warned youths against...

Read More
Mic Mash’s ‘Mtima’ a powerful anthem of heartbreak and revenge-

Mic Mash’s ‘Mtima’ a powerful anthem of heartbreak and revenge

Lilongwe-based artist Mic Mash has made a signific...

Read More
Elon Musk wavulidwa-

Elon Musk wavulidwa

Mpondamatiki Elon Musk, yemweso ndi mwini wa tsamb...

Read More
Paragon restages post-abortion play-

Paragon restages post-abortion play

By Jimmy Chazama In a drive that is aimed at disse...

Read More
Join the union, Mum leader urges musicians-

Join the union, Mum leader urges musicians

Musicians Union of Malawi (Mum) leader Vita Chirwa...

Read More
Veteran musicians need to realign, says Lloyd Phiri-

Veteran musicians need to realign, says Lloyd Phiri

Veteran gospel musician and producer Lloyd Phiri o...

Read More